Ephesians 3:1 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Nchifukwa chake ine Paulo ndimakupemphererani. Ndine womangidwa m'ndende chifukwa chotumikira Khristu ndi kugwirira ntchito inu amene simuli Ayuda.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Chifukwa cha ichi ine Paulo, ndine wandende wa Khristu Yesu chifukwa cha inu amitundu,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Nʼchifukwa chake ine Paulo, ndili wamʼndende wa Khristu Yesu chifukwa cha inu anthu a mitundu ina.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Cifukwa ca ici ine Paulo, ndine wandende wa Kristu Yesu cifukwa ca inu amitundu,