Ephesians 4:12 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ntchito yao inali yakuti akonzeretu anthu a Mulungu kuti akagwire ntchito yotumikira, ndi kulimbitsa Mpingo umene uli thupi la Khristu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
kuti akonzere oyera mtima kuntchito ya utumiki, kumangirira thupi la Khristu;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ntchito yawo ndi kukonza oyera mtima kuti agwire ntchito ya utumiki kuti thupi la Khristu lilimbikitsidwe.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
kuti akonzere oyera mtima: ku nchito ya utumiki, kumangirira thupi la Kristu;