Ephesians 4:6 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pali Mulungu mmodzi amene ali Atate a anthu onse. Iye ali pamwamba pa onse, amagwira ntchito kudzera mwa onse, ndipo ali mwa onse.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Mulungu mmodzi ndi Atate wa onse amene ali pamwamba pa onse, ndi mwa onse, ndi m'kati mwa zonse.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mulungu mmodzi ndi Atate a onse, ndipo ali mwa onse.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mulungu mmodzi ndi Atate wa onse amene ali pamwamba pa onse, ndi mwa onse, ndi m'kati mwa zonse.