Ephesians 5:15 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Samalirani bwino mayendedwe anu. Musayende monga anthu opanda nzeru, koma monga anthu anzeru.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Potero, penyani bwino umo muyendera, si monga opanda nzeru, koma monga anzeru;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Samalani makhalidwe anu, musakhale ngati opanda nzeru koma ngati anzeru.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Potero, penyani bwino umo muyendera, si monga opanda nzeru, koma monga anzeru;