Ephesians 5:16 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mukhale achangu, osataya nthaŵi yanu pachabe, pakuti masiku ano ngoipa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
akuchita machawi, popeza masiku ali oipa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Gwiritsani ntchito mpata uliwonse, chifukwa masiku ano ndi oyipa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
akucita macawi, popeza masiku ali oipa,