Ephesians 5:17 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Nchifukwa chake musakhale opusa, koma dziŵani zimene Ambuye afuna kuti muchite.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Chifukwa chake musakhale opusa, koma dziwitsani chifuniro cha Ambuye nchiyani.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Choncho musakhale opusa, koma mudziwe zimene Ambuye akufuna kuti muchite.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Cifukwa cace musakhale opusa, koma dziwitsani cifuniro ca Ambuye nciani.