Ephesians 5:18 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Musaledzere vinyo, kumeneko nkudzitaya, koma mudzazidwe ndi Mzimu Woyera.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo musaledzere naye vinyo, m'mene muli chitayiko; komatu mudzale naye Mzimu,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Musaledzere ndi vinyo, chifukwa adzawononga moyo wanu. Mʼmalo mwake, mudzazidwe ndi Mzimu Woyera.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo musaledzere naye vinyo, m'mene muli citayiko; komatu mudzale naye Mzimu,