Ephesians 6:7 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Muzitumikira mosangalala, ngati kuti mukutumikira Ambuye, osati anthu chabe.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
akuchita ukapolo ndi kuvomereza mtima, monga kutumikira Ambuye Yesu Khristu, si anthu ai;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Tumikirani ndi mtima wonse, ngati kuti mukutumikira Ambuye, osati anthu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
akucita ukapolo ndi kubvomereza mtima, monga kutumikira Yesu Kristu, si anthu ai;