Esther 2:8 — Compare Translations

3 translations compared side by side

Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo kunali, atamveka mau a mfumu ndi lamulo lake, ndipo atasonkhanidwa anamwali ambiri m'chinyumba cha ku Susa, awasunge Hegai, anamtenga Estere yemwe, alowe m'nyumba ya mfumu, amsunge Hegai wosunga akazi.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Lamulo la mfumu atalilengeza ndi kubwera nawo pamodzi anamwali ambiri ku mzinda wa Susa kuti akasamalidwe ndi Hegai, Estere nayenso anatengedwa kupita naye ku nyumba ya mfumu kuti akasamalidwe ndi Hegai woyangʼanira nyumba yosungiramo akazi uja.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo kunali, atamveka mau a mfumu ndi lamulo lace, ndipo atasonkhanidwa anamwali ambiri m'cinyumba ca ku Susani, awasunge Hege, anamtenga Estere yemwe, alowe m'nyumba ya mfumu, amsunge Hege wosunga akazi.