Esther 3:1 — Compare Translations
3 translations compared side by side
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Zitatha izi, mfumu Ahasuwero anamkuza Hamani mwana wa Hamedata, wa ku Agagi, namkweza, naika mpando wake upose akalonga onse okhala naye.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Zitachitika izi, mfumu Ahasiwero anamukweza Hamani mwana wa Hamedata Mwagagi, anamulemekeza ndikumupatsa mpando wa ulemu kuposa nduna zina zonse.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Zitatha izi, mfumu Ahaswero anamkuza Hamani mwana wa Hamedata, wa ku Agagi, namkweza, naika mpando wace upose akalonga onse okhala naye.