Esther 8:6 — Compare Translations

3 translations compared side by side

Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
pakuti ndidzapirira bwanji pakuchiona choipa chilikudzera a mtundu wanga, kapena ndidzapirira bwanji pakuchiona chionongeko cha fuko langa?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kodi ndingapirire bwanji pamene ndi kuona tsoka likugwera anthu a mtundu wanga? Ndingapirire bwanji pamene abale anga akuwonongedwa?”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
pakuti ndidzapirira bwanji pakuciona coipa cirikudzera amtundu wanga, kapena ndidzapirira bwanji pakuciona cionongeko ca pfuko langa?