Exodus 10:4 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ukakanabe kuŵalola kuti apite, ndikugwetsera dzombe maŵa m'dziko mwako.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
pakuti ukakana kulola anthu anga amuke, taona, mawa ndidzafikitsa dzombe m'dziko lako;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ngati ukana kuwalola, ndigwetsa dzombe mʼdziko lako lino mawa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
pakuti ukakana kulola anthu anga amuke, taona, mawa ndidzafikitsa dzombe m'dziko lako;