Exodus 12:26 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ana anu azidzakufunsani kuti, ‘Kodi mwambo umenewu umatanthauza chiyani?’
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo kudzakhala, pamene ana anu adzanena ndi inu, Kutumikiraku muli nako nkutani?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndipo ana anu akakakufunsani kuti, ‘Mwambo umenewu ukutanthauza chiyani?’
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo kudzakhala, pamene ana anu adzanena ndi inu, Kutumikiraku muli nako nkutani?