Exodus 13:14 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
M'tsogolo mwana wanu wamwamuna adzakufunsani kuti, ‘Kodi zimenezi zikutanthauza chiyani?’ Pamenepo inu mudzayankhe kuti, ‘Chauta adatitulutsa ku Ejipito, ku dziko laukapolo, ndi dzanja lake lamphamvu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo kudzakhala, akakufunsa mwana wako masiku akudzawo ndi kuti, Ichi nchiyani? Ukanene naye, Yehova anatitulutsa m'Ejipito, m'nyumba ya akapolo, ndi dzanja lamphamvu;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Mʼtsogolomo mwana wanu akakafunsa kuti, ‘Zimenezi zikutanthauza chiyani?’ Mukamuwuze kuti, ‘Yehova anatitulutsa mʼdziko la Igupto, dziko la ukapolo ndi dzanja lamphamvu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo kudzakhala, akakufunsa mwana wako masiku akudzawo ndi kuti, Ici nciani? ukanene naye, Yehova anatiturutsa m'Aigupto, m'nyumba ya aka polo, ndi dzanja lamphamvu;