Exodus 15:5 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Nyanja yozamayo idaŵaphimba onse, adamira mpaka pansi pa nyanja ngati miyala.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Nyanja inawamiza; anamira mozama ngati mwala.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Nyanja yakuya inawaphimba; Iwo anamira pansi ngati mwala.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Nyanja inawamiza: Anamira mozama ngati mwala.