Exodus 2:1 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Munthu wina wa fuko la Levi adakwatira mkazi wa fuko lomwelo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo anamuka munthu wa banja la Levi, natenga mwana wamkazi wa Levi.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndipo munthu wina wa fuko la Levi anakwatira mkazi wa fuko lomwelo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo anamuka munthu wa banja la Levi, natenga mwana wamkazi wa Levi.