Exodus 20:3 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Usakhale ndi milungu ina, koma Ine ndekha.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Usakhale nayo milungu ina koma Ine ndekha.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Usakhale ndi milungu ina koma Ine ndekha.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Usakhale nayo milungu yina koma Ine ndekha.