Exodus 22:23 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mukamaŵazunza, Ine ndidzaŵamva iwowo akamalira kwa Ine.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ukawazunza ndi kakuti konse, nakandilirira pang'ono ponse iwowa, ndidzamvadi kulira kwao;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ngati muwazunza ndipo iwo nʼkulirira kwa Ine, ndidzamva kulira kwawo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ukawazunza ndi kakuti konse, nakandilirira pang'ono ponse iwowa, ndidzamvadi kulira kwao;