Exodus 23:32 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Musadzachite nawo chipangano iwowo kapenanso milungu yao.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Usapangana nao, kapena ndi milungu yao.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Musachite pangano ndi iwo kapena ndi milungu yawo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Usapangana nao, kapena ndi milungu yao.