Exodus 27:13 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Chakuvuma, komwe kuli chipata chake, bwalolo likhalenso mamita 23 muufupi mwake.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo m'kupingasa kwake kwa bwalo pa mbali ya kum'mawa, kum'mawa, mukhale mikono makumi asanu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mbali yakummawa, kotulukira dzuwa, kutalika kwa bwalo kukhale mamita 23.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo m'kupingasa kwace kwa bwalo pa mbali ya kum'mawa, kum'mawa, mukhale mikono makumi asanu.