Exodus 30:24 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
makilogaramu asanu ndi limodzi a kasiya (zonsezo potsata miyeso ya ku Nyumba ya Mulungu). Ndipo muwonjeze mafuta okwanira malita anai a olivi.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
ndi kida mazana asanu, monga sekeli la malo opatulika, ndi mafuta a azitona hini limodzi;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
makilogalamu asanu ndi limodzi a mkesha. Zonsezi zikhale malingana ndi muyeso wa ku Nyumba ya Mulungu. Pakhalenso malita anayi a mafuta a olivi.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
ndi kida mazana asanu, monga sekeli la malo opatulika, ndi mafuta a azitona hini limodzi;