Exodus 31:2 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Ndasankha Bezalele mwana wa Uri, mdzukulu wa Huri, wa fuko la Yuda.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Taona ndaitana ndi kumtchula dzina lake, Bezalele, mwana wa Uri, mwana wa Huri, wa fuko la Yuda;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Taona, ndasankha Bezaleli mwana wa Uri, mwana wa Huri, wa fuko la Yuda.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Taona ndaitana ndi kumchula dzina lace, Bezaleli, mwana wa Uri, mwana wa Huri, wa pfuke la Yuda;