Exodus 34:23 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Amuna onse azibwera pamaso pa Ine Chauta, Mulungu wa Aisraele, katatu pa chaka.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Amuna ako onse azioneka pamaso pa Yehova Mulungu, Mulungu wa Israele, katatu chaka chimodzi.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Amuna onse azionekera pamaso pa Yehova Mulungu wa Israeli, katatu pa chaka.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Amuna ako onse azioneka pamaso pa Yehova Mulungu, Mulungu wa Israyeli, katatu caka cimodzi.