Exodus 5:7 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Musaŵapatsenso udzu wa njerwa anthu ameneŵa, monga muja munkachitiramu. Alekeni azikamweta okha udzuwo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Musawapatsanso anthu udzu wakupanga nao njerwa monga kale; apite okha adzifunire udzu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Inu musawapatsenso udzu wopangira njerwa monga mumachitira kale, iwo azipita ndi kukatenga udzu wawo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Musawapatsanso anthu udzu wakupanga nao njerwa monga kale; apite okha adzifunire udzu.