Exodus 9:17 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Koma ukunyozabe anthu anga, osafuna kuŵalola kuti apite.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Kodi udzikwezanso pa anthu anga, ndi kusawalola amuke?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Komabe iwe ukudzitukumula pa anthu anga osawalola kuti atuluke.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Kodi udzikwezanso pa anthu anga, ndi kusawalola amuke?