Ezekiel 10:12 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Matupi ao, misana yao, mapiko ao pamodzi ndi mikombero yonse inai, zonse zinali ndi maso.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo thupi lao lonse, ndi misana yao, ndi manja ao, ndi mapiko ao, ndi njinga zomwe, zinadzala ndi maso pozungulira pao, zingakhale njingazi anai aja anali nazo.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Matupi awo onse, misana yawo, manja awo ndi mapiko awo zinali ndi maso okhaokha, monganso mʼmene inalili mikombero yawo inayi ija.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo thupi lao lonse, ndi misana yao, ndi manja ao, ndi mapiko ao, ndi njinga zomwe, zinadzala ndi maso pozungulira pao, zingakhale njingazi anai aja anali nazo.