Ezekiel 10:17 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Zilengolengo zikaima, mikombero inkaimanso. Zikauluka, mikombero inkapita nawo ndithu, pakuti mzimu wa zilengolengozo ndiwo unkayendetsa mikomberoyo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pakuima iwo zinaima izi, ndi pakukwera iwo izi zinakwera pamodzi nao; pakuti mzimu wa zamoyozo unali mwa izo.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Akerubiwo ankati akayima, mikombero inkayimanso. Ngati akerubiwo auluka, mikomberoyo inkapita nawo chifukwa mzimu wa zamoyozo ndiwo unkayendetsa mikomberoyo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pakuima iwo zinaima izi, ndi pakukwera iwo izi zinakwera pamodzi nao; pakuti mzimu wa zamoyozo unali mwa izo.