Ezekiel 11:21 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Koma amene mitima yao yazama m'zonyansa ndi zoipa zinazo, ndidzaŵalanga chifukwa cha zonse zimene adachita. Ndikutero Ine Chauta.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma iwo amene mtima wao unatsata mtima wa zonyansa zao, ndi zoipitsitsa zao, ndidzawabwezera njira yao pamtu pao, ati Yehova Mulungu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Koma kunena za amene akupembedza mafano oyipa ndi onyansa, ndidzawalanga chifukwa cha zimene achita. Ndikutero Ine Ambuye Yehova.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma iwo amene mtima wao unatsata mtima wa zonyansa zao, ndi zoipitsitsa zao, ndidzawabwezera njira yao pamtu pao, ati Yehova Mulungu.