Ezekiel 11:3 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Iwo amati, ‘Nthaŵi sinafike yoti nkumanga nyumba. Mzindawu uli ngati mphika umene uli pa moto, ifeyo tili ngati nyama imene ili mumphikamo.’
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
ndiwo akuti, siinafike nyengo yakumanga nyumba; mudzi uwu ndi mphika, ife ndife nyama.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Iwo amawuza anthu kuti, ‘Nthawi sinafike yoti timange Nyumba? Mzindawu uli ngati mʼphika umene uli pa moto ndipo ife tili ngati nyama mu mʼphikamo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
ndiwo akuti, siinafike nyengo yakumanga nyumba; mudzi uwu ndi mphika, ife ndife nyama.