Ezekiel 12:15 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Motero adzadziŵa kuti Ine ndine Chauta, ndikadzaŵamwaza pakati pa mitundu yachilendo ndi kuŵabalalitsa ku maiko ambiri.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Motero adzadziwa kuti Ine ndine Yehova, pakuwamwaza Ine mwa amitundu, ndi kuwabalalitsa m'maiko.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Iwo adzadziwa kuti Ine ndine Yehova, ndikadzawamwaza pakati pa anthu a mitundu ina ndi kuwabalalitsira ku mayiko ena.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Motero adzadziwa kuti Ine ndine Yehova, pakuwamwaza Ine mwa amitundu, ndi kuwabalalitsa m'maiko.