Ezekiel 13:15 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndimo m'mene ndidzagwiritsire ntchito mkwiyo wanga pa khomalo ndi pa amene ankalipaka njereza aja. Apo ndidzakuuzani kuti, ‘Khoma lagwa, amene ankalimata aja nawonso agwera kumodzi.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
M'mwemo ndidzakwaniritsa ukali wanga pa lingalo, ndi pa iwo analimata ndi dothi losapondeka, ndipo ndidzati kwa inu, Lingalo palibe, ndi olimata palibe,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kotero ndidzagwiritsa ntchito mkwiyo wanga pa khomali ndi pa amene analipaka njereza. Pambuyo pake ndidzakuwuzani kuti, ‘Khoma lagwa pamodzi ndi amene analipaka njereza.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
M'mwemo ndidzakwaniritsa ukali wanga pa lingalo, ndi pa iwo analimata ndi dothi losapondeka, ndipo ndidzati kwa inu, Lingalo palibe, ndi olimata palibe,