Ezekiel 14:19 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Mwina ndikadatumiza mliri m'dziko limenelo, ndi kuwonetsa ukali wanga pokhetsa magazi ndi kuwononga anthu ndi nyama zomwe.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Kapena ndikatumizira dzikolo mliri, ndi kulitsanulira ukali wanga ndi mwazi, kulidulira munthu ndi nyama;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Kapena ndikanatumiza mliri mʼdzikomo ndi kuonetsa ukali wanga pokhetsa magazi, kuwononga anthu ake ndi nyama zomwe.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Kapena ndikatumizira dzikolo mliri, ndi kulitsanulira ukali wanga ndi mwazi, kulidulira munthu ndi nyama;