Ezekiel 14:21 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Zimene ndikunena Ine Ambuye Chauta ndi izi: Kudzakhala zoopsa kwambiri pamene ndidzagwetsa pa Yerusalemu zilango zanga zinai izi: nkhondo, njala, zilombo ndi mliri, kuti ziwononge anthu ndi nyama.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pakuti atero Ambuye Yehova, Kopambana kotani nanga ndikatumizira Yerusalemu maweruzo anga anai owawa, lupanga, njala, zilombo zoipa, ndi mliri, kuudulira anthu ndi nyama?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Pakuti Ambuye Yehova akuti: Kudzakhala zoopsa kwambiri pamene ndidzatumiza pa Yerusalemu zilango zanga zinayi izi: lupanga, njala, zirombo ndi mliri kuti ziwononge anthu ake ndi nyama zomwe!
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pakuti atero Ambuye Yehova, Kopambana kotani nanga ndikatumizira Yerusalemu maweruzo anga anai owawa, lupanga, njala, zirombo zoipa, ndi mliri, kuudulira anthu ndi nyama?