Ezekiel 16:21 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
apa ukupha ana anga ndi kuŵapereka kwa mafano ako?
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
kuti unawapha ana anga ndi kuwapereka, pakuwapititsa pamoto?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
kuti uziphanso ana anga ndi kuwapereka ngati nsembe kwa mafano akowo?
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
kuti unawapha ana anga ndi kuwapereka, pakuwapititsa pamoto?