Ezekiel 16:25 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Udamanga nsanja zakozo pa mseu uliwonse. Pamenepo udanyazitsa kukongola kwako, podzipereka kwa aliyense wodutsapo. Wakhala ukuchita zigololo kosaŵerengeka.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Unamanga chiunda chako pa mphambano zilizonse, ndipo unanyansitsa kukongola kwako, ndi kutukula mapazi ako kwa yense wopitako, ndi kuchulukitsa chigololo chako.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Pa msewu uliwonse wamanga nsanjazo. Motero wanyazitsa kukongola kwako podzipereka kwa aliyense amene adutsapo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Unamanga ciunda cako pa mphambano ziri zonse, ndipo unanyansitsa kukongola kwako, ndi kutukula mapazi ako kwa yense wopitako, ndi kucurukitsa cigololo cako.