Ezekiel 16:3 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Umuuze kuti, Ambuye Chauta akukuuza kuti, ‘Kanani ndi dziko la makolo ako, ndipo udabadwira kumeneko. Atate ako anali Mwamori, amai ako anali Muhiti.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Atero Ambuye Yehova kwa Yerusalemu, Chiyambi chako ndi kubadwa kwako ndiko kudziko la Akanani; atate wako anali Mwamori, ndi mai wako Muhiti.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Umuwuze kuti, ‘Ambuye Yehova akukuwuza, iwe Yerusalemu kuti: Kwawo kwa makolo ako ndi ku Kanaani ndipo iwe unabadwira komweko. Abambo ako anali Mwamori, amayi ako anali Mhiti.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Atero Ambuye Yehova kwa Yerusalemu, Ciyambi cako ndi kubadwa kwako ndiko ku dziko la Akanani; atate wako anali M-amori, ndi mai wako Mhiti.