Ezekiel 16:40 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Adzatuma gulu la anthu kuti akuponye miyala ndi kukudula pafupipafupi ndi malupanga ao.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo adzamemezera iwe msonkhano, nadzakuponya miyala, ndi kukupyoza ndi malupanga ao.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Iwo adzabweretsa gulu la anthu limene lidzakuponya miyala ndi kukutematema ndi malupanga awo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo adzamemezera iwe msonkhano, nadzakuponya miyala, ndi kukupyoza ndi malupanga ao.