Ezekiel 18:10 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Mwina munthu wotero nkubala mwana amene ntchito yake nkuba ndiponso kupha anthu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Akabala mwana ndiye mkhungu, wokhetsa mwazi, wochita chimodzi cha izi,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Tiyerekeze kuti munthu wolungama chotere wabala mwana chimbalangondo amene amakhalira kupha anthu ndi kuchita zinthu zina zotere.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Akabala mwana ndiye mkhungu, wokhetsa mwazi, wocita cimodzi ca izi,