Ezekiel 18:11 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Iye amachita zambiri zimene bambo wake sadachitepo. Amadyera nao ku zitunda zachipembedzo, amaipitsa mkazi wa munthu wina,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
wosachita zabwino zonse zija, koma anadyanso pamapiri, naipsa mkazi wa mnansi wake,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Iye nʼkumachita zinthu zimene ngakhale abambo ake sanachitepo. “Amadyera nawo ku mapiri achipembedzo. Amayipitsa mkazi wa mnzake.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
wosacita zabwino zonse zija, koma anadyanso pamapiri, naipsa mkazi wa mnansi wace,