Ezekiel 18:13 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Amakongoza kuti apezepo phindu, ndipo kuti alandire chiwongoladzanja. Kodi munthu wotereyu nkukhala ndi moyo? Ai ndithu, sadzakhala ndi moyo. Chifukwa adachita zoipa zonsezi, adzaphedwa, ndicho chilango chomuyenerera.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
napereka molira phindu, nalandira choonjezerapo; adzakhala ndi moyo uyu kodi? Sadzakhala ndi moyo, anachita zonyansa izi zonse; kufa adzafadi, mwazi wake umkhalira.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Iye amakongoletsa mwa katapira ndipo amalandira chiwongoladzanja chachikulu. Kodi munthu wotereyu nʼkukhala ndi moyo? Ayi ndithu! Chifukwa wachita zinthu zonyansa zonsezi, adzaphedwa ndipo adzalandira chilango chomuyenera.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
napereka molira phindu, nalandira coonjezerapo; adzakhala ndi moyo uyu kodi? sadzakhala ndi moyo, anacita zonyansa izi zonse; kufa adzafadi, niwazi wace umkhalira.