Ezekiel 18:15 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Sapembedza mafano a ku Israele, saipitsa mkazi wa munthu wina,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
wosadya pamapiri, kapena kukweza maso ake kumafano a nyumba ya Israele, wosaipsa mkazi wa mnansi wake,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Sadyera nawo pa mapiri achipembedzo. Sapembedza mafano a ku Israeli. Sayipitsa mkazi wa mnzake.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
wosadya pamapiri, kapena kukweza maso ace ku mafano a nyumba ya Israyeli, wosaipsa mkazi wa mnansi wace,