Ezekiel 18:2 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Chifukwa chiyani anthu a ku Israelenu mumakonda kubwerezabwereza mwambi uja wakuti, ‘Nkhuyu zodya akulu zidapota ndi ana omwe?’
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Mutani inu ndi kunena mwambi uwu za dziko la Israele, wakuti, Atate adadya mphesa zosacha, ndi mano a ana ayayamira.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Kodi anthu inu mumatanthauza chiyani mukamabwerezabwereza kunena mwambi uwu wokhudza dziko la Israeli kuti: “ ‘Nkhuyu zodya akulu zimapota ndi ana omwe?’ ”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mutani inu ndi kunena mwambi uwu za dziko la Israyeli, wakuti, Atate adadya mphesa zosacha, ndi mano a ana ayayamira.