Ezekiel 18:22 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Zoipa zake zonse zidzakhululukidwa. Adzakhala ndi moyo chifukwa cha ntchito zake zolungama.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Nnena chimodzi chonse cha zolakwa zake zonse adazichita chidzakumbukika chimtsutse; m'chilungamo chake adachichita adakhala ndi moyo.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Zoyipa zake zonse zidzakhululukidwa. Chifukwa cha zinthu zolungama zimene anazichita adzakhala ndi moyo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Nnena cimodzi conse ca zolakwa zace zonse adazicita cidzakumbukika cimtsutse; m'cilungamo cace adacicita adakhala ndi moyo.