Ezekiel 18:27 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Komanso munthu woipa akaleka zoipa zake, namachita zoyenera, adzapulumutsa moyo wake.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo woipayo akatembenukira kuleka choipa chake adachichita, nakachita chiweruzo ndi chilungamo, adzapulumutsa moyo wake.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Koma ngati munthu woyipa aleka zoyipa zake zimene anazichita ndi kuyamba kuchita zimene ndi zolungama ndi zolondola, iye adzapulumutsa moyo wake.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo woipayo akatembenukira kuleka coipa cace adacicita, nakacita ciweruzo ndi cilungamo, adzapulumutsa moyo wace.