Ezekiel 18:29 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Komabe Aisraele akunena kuti zochita za Ambuye nzosalungama. Pepani, Aisraele inu, ndinu amene mumachita zosalungama, osati Ine.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma nyumba ya Israele imanena, Njira ya Ambuye njosayenera. Inu, nyumba ya Israele, kodi njira zanga nzosayenera? Njira zanu si ndizo zosayenera?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Komabe Aisraeli akunena kuti, ‘Zimene Ambuye amachita ndi zopanda chilungamo.’ Kodi zochita zanga ndizo zopanda chilungamo, inu Aisraeli? Kodi si zochita zanu zimene ndi zopanda chilungamo?
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma nyumba ya Israyeli imanena, Njira ya Ambuye njosayenera, Inu, nyumba ya Israyeli, kodi njira zanga nzosayenera? njira zanu si ndizo zosayenera?