Ezekiel 18:5 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Tiyese kuti pali munthu wabwino amene amatsata malamulo ndi kuchita zabwino.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma munthu akakhala wolungama, nakachita chiweruzo ndi chilungamo,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Tiyerekeze kuti pali munthu wolungama amene amachita zolungama ndi zolondola.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma munthu akakhala wolungama, nakacita ciweruzo ndi cilungamo,