Ezekiel 19:6 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Unkayendayenda pakati pa mikango inzake, pakuti unali mkango wokhwima. Udaphunzira kugwira nyama, nuyamba kudya anthu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo unayendayenda pakati pa mikango, nukhala msona, nuphunzira kugwira nyama, nulusira anthu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Unkayendayenda pakati pa mikango inzake, pakuti tsopano unali mkango wamphamvu. Unaphunzira kugwira nyama ndipo unayamba kudya anthu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo unayendayenda pakati pa mikango, nukhala msona, nuphunzira kugwira nyama, nulusira anthu.