Ezekiel 2:7 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Popeza kuti iwowo ngaupandu, kaya akamvera kaya akakana, udzaŵauze ndithu mau anga.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo ukanene nao mau anga, ngakhale akamva kapena akaleka kumva; pakuti iwo ndiwo opanduka.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ukawawuze ndithu mawu anga, kaya akamva kaya sakamva. Paja anthuwa ndi awupandu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo ukanene nao mau anga, ngakhale akamva kapena akaleka kumva; pakuti iwo ndiwo opanduka.