Ezekiel 20:18 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Ndidalamula ana ao m'chipululu kuti asatsate malangizo a makolo ao, asamvere malamulo ao, kapena kudziipitsa ndi mafano ao.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo ndinati kwa ana ao m'chipululu, Musamayenda m'malemba a atate anu, musawasunga maweruzo ao, kapena kudzidetsa ndi mafano ao;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Tsono kwa ana awo mʼchipululu ndinati, ‘Musatsatire malangizo a makolo anu kapena kusunga malamulo awo kapena kudziyipitsa ndi mafano awo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo ndinati kwa ana ao m'cipululu, Musamayenda m'malemba a atate anu, musawasunga maweruzo ao, kapena kudzidetsa ndi mafano ao;