Ezekiel 20:23 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndidachita kulumbira m'chipululu nditakweza dzanja, kuti ndidzaŵabalalitsa pakati pa mitundu ya anthu ndi kuŵamwazira ku maiko akutali,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndinawakwezeranso dzanja langa m'chipululu, kuti ndidzawabalalitsa mwa amitundu, ndi kuwamwaza m'maiko;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Choncho ndinalumbira mʼchipululu, nditakweza dzanja langa, kuti ndidzawabalalitsa pakati pa anthu a mitundu ina ndi kuwamwazira ku mayiko akutali,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
kuti ndidzawabalalitsa mwa amitundu, ndi kuwamwaza m'maiko;